Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Tinamva za mmene Yehova anaphwetsera madzi a Nyanja Yofiira pamaso panu, mutatuluka m’dziko la Iguputo.+ Tinamvanso za mmene munaphera+ mafumu awiri a Aamori, Sihoni+ ndi Ogi,+ kutsidya kwa Yorodano.

  • Salimo 66:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Anasandutsa nyanja kukhala malo ouma,+

      Anthu anawoloka mtsinje mwa kuyenda ndi mapazi awo.+

      Pamenepo tinayamba kusangalala mwa iye.+

  • Salimo 106:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Choncho anadzudzula Nyanja Yofiira, ndipo pang’onopang’ono nyanjayo inauma.+

      Pamenepo anawayendetsa kudutsa pakati pa madzi akuya ngati akuwayendetsa m’chipululu.+

  • Salimo 114:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Nyanja inaona ndipo inathawa.+

      Yorodano anabwerera m’mbuyo.+

  • Yesaya 51:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kodi si iwe amene unaumitsa nyanja, amene unaumitsa madzi akuya kwambiri?+ Si iwe kodi amene unasandutsa pansi pa nyanja kukhala njira yoti anthu owomboledwa awolokerepo?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena