Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 14:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Mose anauza anthuwo kuti: “Musachite mantha.+ Chilimikani ndi kuona chipulumutso cha Yehova chimene akuchitireni lero.+ Pakuti Aiguputo amene mukuwaona lerowa simudzawaonanso, ndithu, simudzawaonanso.+

  • Salimo 106:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndiyeno madzi anamiza adani awo,+

      Moti panalibe ngakhale mmodzi amene anapulumuka.+

  • Salimo 136:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Amenenso anakutumulira Farao ndi gulu lake lankhondo m’Nyanja Yofiira:+

      Pakuti kukoma mtima kwake kosatha kudzakhalapobe mpaka kalekale.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena