Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Loti anawaumiriza kwambiri+ moti mpaka iwo anapita naye kunyumba kwake. Kumeneko anawakonzera phwando,+ n’kuwaphikira mikate yopanda chofufumitsa,+ ndipo anadya.

  • Genesis 24:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Atangomuona anamuuza kuti: “Tabwerani, inu wodalitsika wa Yehova.+ Bwanji mwangoima kunja kuno? Inetu ndakonza kale malo kunyumbaku, a inu ndi a ngamilazi.”

  • Yobu 31:32
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 32 Palibe mlendo amene ankagona panja usiku.+

      Zitseko zanga ndinkazisiya zotsegula kwa odutsa m’njira.

  • Aroma 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Gawanani ndi oyera malinga ndi zosowa zawo.+ Khalani ochereza.+

  • Aheberi 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Musaiwale kuchereza alendo,+ pakuti potero, ena anachereza angelo mosadziwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena