Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 19:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Koma Loti anawaumiriza kwambiri+ moti mpaka iwo anapita naye kunyumba kwake. Kumeneko anawakonzera phwando,+ n’kuwaphikira mikate yopanda chofufumitsa,+ ndipo anadya.

  • Oweruza 19:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Atatero anatengera Mlevi uja kunyumba kwake+ ndipo anapatsa abulu ake aja chakudya.+ Ndiyeno anasamba mapazi awo+ n’kuyamba kudya ndi kumwa.

  • Mateyu 25:35
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 35 Pakuti ine ndinamva njala koma inu munandipatsa chakudya.+ Ndinamva ludzu koma inu munandipatsa chakumwa. Ndinali mlendo koma inu munandilandira bwino.+

  • Aheberi 13:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Musaiwale kuchereza alendo,+ pakuti potero, ena anachereza angelo mosadziwa.+

  • 1 Petulo 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Muzicherezana popanda kudandaula.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena