Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 19:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma Mulungu anati: “Tuluka, kaime paphiri pamaso pa Yehova.”+ Kenako Yehova anadutsa,+ ndipo kunawomba chimphepo champhamvu chomwe chinali kung’amba mapiri ndi kuphwanya matanthwe pamaso pa Yehova.+ (Yehova sanali mumphepoyo.) Pambuyo pa chimphepocho, kunachita chivomezi.+ (Yehova sanali m’chivomezicho.)

  • Salimo 68:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dziko lapansi linagwedezeka,+

      Kumwamba kunagwa mvula chifukwa cha inu Mulungu,+

      Phiri ili la Sinai linagwedezeka chifukwa cha inu Mulungu,+ Mulungu wa Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena