Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 14:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako anthu amene anali kutchire mumsasa ndi anthu onse kumudzi wa asilikaliwo anayamba kunjenjemera.+ Anthu olanda katundu+ nawonso anali kunjenjemera, ndipo nthaka inayamba kugwedezeka.+ Zimenezi zinali zochokera kwa Mulungu.+

  • Yobu 9:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Amachititsa dziko lapansi kunjenjemera pamalo ake,

      Mwakuti zipilala+ zake zimagwedezeka.

  • Salimo 68:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Dziko lapansi linagwedezeka,+

      Kumwamba kunagwa mvula chifukwa cha inu Mulungu,+

      Phiri ili la Sinai linagwedezeka chifukwa cha inu Mulungu,+ Mulungu wa Isiraeli.+

  • Nahumu 1:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Mapiri agwedezeka chifukwa cha iye ndipo zitunda zasungunuka.+

      Dziko lapansi, nthaka ndi zinthu zonse zokhala m’dzikomo zidzanjenjemera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena