Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 1:50
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 50 Adoniya anachita mantha chifukwa cha Solomo. Choncho ananyamuka n’kupita kukagwira nyanga za guwa lansembe.+

  • 1 Mafumu 2:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Kenako Mfumu Solomo inauzidwa kuti: “Yowabu wathawira kuchihema cha Yehova, ndipo ali pambali pa guwa lansembe.” Choncho Solomo anatuma Benaya mwana wa Yehoyada, kuti: “Pita ukamuphe!”+

  • 2 Mafumu 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma wansembe Yehoyada analamula atsogoleri a magulu a asilikali 100, kapena kuti asilikali osankhidwa,+ kuti: “M’chotseni pakati pa mizere ya anthu! Aliyense amene angam’tsatire pambuyo pake aphedwe ndi lupanga!”+ Popeza wansembeyo anali atanena kuti: “Muonetsetse kuti asaphedwere m’nyumba ya Yehova.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena