-
2 Mafumu 11:4Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
4 M’chaka cha 7, Yehoyada+ anatumiza uthenga kwa atsogoleri a magulu a asilikali 100 olondera mfumu Achikariya,+ ndiponso kwa atsogoleri a magulu a asilikali 100 othamanga.+ Anawaitanitsa kuti abwere kwa iye kunyumba ya Yehova ndipo anachita nawo pangano+ n’kuwalumbiritsa+ kunyumba ya Yehova. Kenako anawaonetsa mwana wa mfumu uja.
-