Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Mafumu 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma wansembe Yehoyada analamula atsogoleri a magulu a asilikali 100, kapena kuti asilikali osankhidwa,+ kuti: “M’chotseni pakati pa mizere ya anthu! Aliyense amene angam’tsatire pambuyo pake aphedwe ndi lupanga!”+ Popeza wansembeyo anali atanena kuti: “Muonetsetse kuti asaphedwere m’nyumba ya Yehova.”

  • 2 Mafumu 11:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Atatero anauza atsogoleri a magulu a asilikali 100, asilikali olondera mfumu Achikariya,+ asilikali othamanga,+ ndi anthu onse a m’dzikolo, kuti aperekeze mfumuyo kuchokera kunyumba ya Yehova. Anthuwo anadzera njira ya pachipata+ cha asilikali othamanga, mpaka anafika kunyumba ya mfumu. Kenako mfumuyo inakhala pampando wachifumu+ wa mafumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena