Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 34:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Kuti achititse kulira kwa wonyozeka kupita kwa iye.

      Choncho iye amamva kulira kwa osautsika.+

  • Salimo 10:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Kuti muweruze mwana wamasiye komanso woponderezedwa.+

      Mudzatero kuti munthu wamba wochokera kufumbi asachititsenso anthu ena kunjenjemera.+

  • Luka 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndithu, ngakhale kuti Mulungu amalezera mtima+ osankhidwa ake, kodi sadzaonetsetsa kuti chilungamo+ chachitika kwa iwo, amene amafuulira kwa iye usana ndi usiku?

  • Yakobo 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Tamverani! Malipiro a anthu amene anagwira ntchito+ yokolola m’minda yanu, amene inu simunapereke,+ akufuula ndipo kufuula kwa okololawo kofuna thandizo+ kwafika m’makutu+ a Yehova wa makamu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena