Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Mlaliki 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngakhale m’chipinda chako, usanenere mfumu zoipa,+ ndipo m’zipinda zimene umagona usanenere zoipa aliyense wolemera,+ chifukwa cholengedwa chouluka chikanena mawu ako ndipo chinachake chokhala ndi mapiko chikaulula zimene wanena.+

  • Machitidwe 23:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Pamenepo Paulo anati: “Abale, sindinadziwe kuti ndi mkulu wa ansembe. Pakuti Malemba amati, ‘Wolamulira wa anthu a mtundu wako usamunenere zachipongwe.’”+

  • 2 Petulo 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 koma makamaka anthu amene amafunafuna kugonana ndi anthu ena n’cholinga choti awaipitse,+ ndiponso amene amanyoza owalamulira.+

      Anthu amenewa ndi opanda mantha ndiponso ndi omva zawo zokha, ndipo sanjenjemera ndi anthu aulemerero. M’malomwake, amalankhula zinthu zowanyoza.+

  • Yuda 8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Ngakhale zili choncho, anthu amenewanso, pokonda zongolota,+ akuipitsa matupi ndi kunyalanyaza ulamuliro+ ndipo amalankhula zonyoza amene ali ndi ulemerero.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena