2 Mukapanda kumvera,+ ndiponso ngati simuganizira nkhani imeneyi mumtima mwanu+ kuti mulemekeze dzina langa,+ ndidzakutumizirani temberero+ ndi kutemberera madalitso anu.+ Ndatemberera dalitso la aliyense wa inu chifukwa simunaganizire nkhani imeneyi mumtima mwanu,” watero Yehova wa makamu.