Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 81:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Koma anthu anga sanamvere mawu anga.+

      Ndipo Isiraeli sanasonyeze kuti ndi wofunitsitsa kundimvera.+

  • Yesaya 42:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Choncho Mulungu anali kuwakhuthulira mkwiyo, ukali wake, ndi nkhondo yoopsa.+ Nkhondoyo inali kuwapsereza+ koma iwo sanazindikire.+ Inapitiriza kuwatentha koma iwo sanaganizire chilichonse mumtima mwawo.+

  • Yesaya 57:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Kodi unachita mantha ndi ndani kuti uyambe kuopa,+ mpaka kuyamba kunama?+ Koma sunakumbukire ine.+ Palibe chimene unaganizira mumtima mwako.+ Popeza ine ndinakhala chete ndipo sindinachitepo kanthu pa zochita zako,+ iweyo sunali kundiopa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena