Ekisodo 34:9 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 9 Kenako iye anati: “Tsopano ngati mwandikomera mtima, inu Yehova, chonde, Yehova ayende nafe pakati pathu,+ chifukwa anthuwa ndi ouma khosi,+ ndipo mutikhululukire zolakwa zathu ndi machimo athu,+ ndi kutitenga kukhala chuma chanu.”+ Levitiko 4:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ng’ombeyo azichita nayo ngati mmene amachitira ndi ng’ombe ya nsembe yamachimo ija. Azichita momwemo. Ndipo wansembe aziwaphimbira machimo+ awo kuti akhululukidwe. Levitiko 6:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Ndiyeno wansembe aziphimba machimo+ a munthuyo pamaso pa Yehova, ndipo azikhululukidwa chilichonse mwa zonse zimene angachite zom’palamulitsa.” Levitiko 19:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Ndiyeno wansembe aziphimba tchimo limene munthuyo wachita. Azitero popereka kwa Yehova nkhosa yamphongo ya nsembe ya kupalamula ija. Pamenepo munthuyo azikhululukidwa tchimo lakelo.+
9 Kenako iye anati: “Tsopano ngati mwandikomera mtima, inu Yehova, chonde, Yehova ayende nafe pakati pathu,+ chifukwa anthuwa ndi ouma khosi,+ ndipo mutikhululukire zolakwa zathu ndi machimo athu,+ ndi kutitenga kukhala chuma chanu.”+
20 Ng’ombeyo azichita nayo ngati mmene amachitira ndi ng’ombe ya nsembe yamachimo ija. Azichita momwemo. Ndipo wansembe aziwaphimbira machimo+ awo kuti akhululukidwe.
7 Ndiyeno wansembe aziphimba machimo+ a munthuyo pamaso pa Yehova, ndipo azikhululukidwa chilichonse mwa zonse zimene angachite zom’palamulitsa.”
22 Ndiyeno wansembe aziphimba tchimo limene munthuyo wachita. Azitero popereka kwa Yehova nkhosa yamphongo ya nsembe ya kupalamula ija. Pamenepo munthuyo azikhululukidwa tchimo lakelo.+