Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 10:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Musachoke pakhomo la chihema chokumanako kuopera kuti mungafe,+ chifukwa mwadzozedwa ndi mafuta odzozera a Yehova.”+ Choncho iwo anachita monga mwa mawu a Mose.

  • Levitiko 21:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma asayandikire nsalu yotchinga+ ndiponso guwa lansembe,+ chifukwa iye ali ndi chilema.+ Asaipitse malo anga opatulika,+ chifukwa ine ndine Yehova amene ndikuwapatula kuti akhale oyera.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena