Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 7:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Koma ngati nyama iliyonse ya nsembe yachiyanjano yadyedwa pa tsiku lachitatu, wopereka nsembeyo sadzayanjidwa ndi Mulungu.+ Nsembe yakeyo sadzapindula nayo.+ Idzakhala chinthu chonyansa, ndipo amene wadyako nsembeyo adzadziyankhira mlandu wa cholakwa chake.+

  • Levitiko 23:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndipo wansembe aziweyulira mtolowo uku ndi uku+ pamaso pa Yehova kuti Mulungu akuyanjeni. Sabata likatha, ndiyeno tsiku lotsatira, wansembe aziweyulira mtolowo uku ndi uku.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena