Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 3:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndipo wansembe azitentha+ zinthu zonsezi paguwa lansembe monga chakudya,+ kuti chikhale nsembe yotentha ndi moto yoperekedwa kwa Yehova.

  • Levitiko 21:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Azikhala oyera kwa Mulungu wawo+ ndipo asaipitse dzina la Mulungu wawo,+ chifukwa iwowa amapereka nsembe zotentha ndi moto zoperekedwa kwa Yehova, mkate wa Mulungu wawo,+ choncho azikhala oyera.+

  • Numeri 28:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mofanana ndi zimenezi, muziperekanso nsembe yotentha ndi moto tsiku lililonse kwa masiku 7, monga chakudya+ cha Yehova, monganso nsembe yafungo lokhazika mtima pansi kwa iye.+ Muziipereka limodzi ndi nsembe yopsereza ya tsiku ndi tsiku, ndi nsembe yake yachakumwa.

  • Malaki 1:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “‘Mwalinyoza mwa kupereka nsembe zodetsedwa paguwa langa lansembe.’+

      “‘Inu mukunena kuti: “Takudetsani motani?”’

      “‘Mwandidetsa ponena kuti: “Tebulo+ la Yehova ndi lonyozeka.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena