Ekisodo 34:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 “Muzichita chikondwerero cha masabata ndi tirigu woyamba kucha pa nyengo yokolola tiriguyo.+ Muzichitanso chikondwerero cha zokolola kumapeto kwa chaka.+ Levitiko 23:16 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 16 Kuchokera pa tsiku limene sabata la 7 lakwanira, pazidutsa masiku 50,+ ndipo muzipereka nsembe yambewu zatsopano+ kwa Yehova. Levitiko 23:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Muzilengeza+ pa tsiku lomweli kuti muchite msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse yolemetsa. Limeneli ndi lamulo mpaka kalekale kulikonse kumene mungakhale m’mibadwo yanu yonse. Deuteronomo 16:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Ndiyeno uzichitira Yehova Mulungu wako+ chikondwerero cha masabata, popereka nsembe zaufulu zimene ungathe, monga mmene Yehova Mulungu wako angakudalitsire.+ Machitidwe 2:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Tsopano pa tsiku la chikondwerero cha Pentekosite,+ onse anali atasonkhana pamalo amodzi.
22 “Muzichita chikondwerero cha masabata ndi tirigu woyamba kucha pa nyengo yokolola tiriguyo.+ Muzichitanso chikondwerero cha zokolola kumapeto kwa chaka.+
16 Kuchokera pa tsiku limene sabata la 7 lakwanira, pazidutsa masiku 50,+ ndipo muzipereka nsembe yambewu zatsopano+ kwa Yehova.
21 Muzilengeza+ pa tsiku lomweli kuti muchite msonkhano wopatulika ndipo musamagwire ntchito iliyonse yolemetsa. Limeneli ndi lamulo mpaka kalekale kulikonse kumene mungakhale m’mibadwo yanu yonse.
10 Ndiyeno uzichitira Yehova Mulungu wako+ chikondwerero cha masabata, popereka nsembe zaufulu zimene ungathe, monga mmene Yehova Mulungu wako angakudalitsire.+