-
Yesaya 58:5Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
5 Kodi kusala kudya kumene ine ndasankha kukhale kotere? Kodi likhale tsiku loti munthu wochokera kufumbi azisautsa moyo wake?+ Kodi likhale tsiku loti munthu aziweramitsa mutu wake ngati udzu, ndiponso loti aziyala chiguduli ngati bedi lake n’kuwazapo phulusa?+ Kodi limeneli ndi limene mumalitcha tsiku losala kudya ndi lovomerezeka kwa Yehova?+
-