Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 2:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 “Chigawo cha mafuko atatu cha Yuda ndi asilikali awo, chizimanga msasa wawo kum’mawa kotulukira dzuwa. Mtsogoleri wa ana a Yuda ndi Naasoni,+ mwana wa Aminadabu.

  • Numeri 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 “Chigawo cha mafuko atatu cha Rubeni+ ndi asilikali awo, chizimanga msasa wawo kum’mwera. Mtsogoleri wa ana a Rubeni ndi Elizuri,+ mwana wa Sedeuri.

  • Numeri 2:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Chigawo cha mafuko atatu cha Efuraimu+ ndi asilikali awo, chizimanga msasa wawo kumadzulo. Mtsogoleri wa ana a Efuraimu ndi Elisama,+ mwana wa Amihudi.

  • Numeri 2:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 “Chigawo cha mafuko atatu cha Dani ndi asilikali awo, chizimanga msasa wawo kumpoto. Mtsogoleri wa ana a Dani ndi Ahiyezeri,+ mwana wa Amisadai.

  • Numeri 2:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Ana a Isiraeli anachita zonse monga mmene Yehova analamulira Mose.+ Dongosolo limene analitsatira pomanga misasa yawo m’zigawo za mafuko atatu,+ n’limenenso anatsatira posamuka,+ aliyense m’banja lake malinga ndi nyumba ya makolo ake.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena