Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 4:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Uwerenge kuyambira azaka 30 mpaka 50, onse olowa m’gulu la ogwira ntchito pachihema chokumanako.+

  • 1 Mbiri 6:48
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 48 Abale awo Alevi+ ndiwo anapatsidwa utumiki wonse+ wa pachihema chopatulika, chimene chili nyumba ya Mulungu woona.

  • 1 Mbiri 23:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Amenewa ndiwo anali ana a Levi potsata nyumba ya makolo awo.+ Iwowa anali atsogoleri a nyumba ya makolo awo, ndipo mmodzi ndi mmodzi anapatsidwa udindo potsata mndandanda wa mayina awo. Amenewa anali oti azigwira ntchito yotumikira+ panyumba ya Yehova kuyambira azaka 20 kupita m’tsogolo.+

  • 1 Mbiri 28:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Anam’patsanso malangizo okhudza magulu+ a ansembe ndi a Alevi, ntchito yonse yokhudza utumiki wa panyumba ya Yehova, ndiponso malangizo okhudza ziwiya zonse za utumiki wa panyumba ya Yehova.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena