Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yoswa 6:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Ndiyeno pa nthawiyo, Yoswa analumbira kuti: “Adzakhale wotembereredwa pamaso pa Yehova munthu amene adzamangenso mzinda wa Yerikowu. Akadzangoyala maziko ake, mwana wake woyamba adzafe, ndipo akadzaika zitseko zake za pachipata, mwana wake wotsiriza adzafe.”+

  • 1 Samueli 14:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Motero amuna a Isiraeli anatopa kwambiri pa tsiku limenelo, komabe Sauli analumbirira+ anthuwo kuti: “Munthu aliyense wodya mkate dzuwa lisanalowe, komanso ndisanabwezere+ adani anga, ndi wotembereredwa!” Choncho panalibe aliyense mwa anthuwo amene anadya mkate.+

  • 1 Mafumu 8:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 “Munthu akachimwira mnzake,+ wochimwiridwayo n’kulumbiritsa*+ wochimwayo pofuna kutsimikiza kuti sanachimwedi, ndiyeno wochimwayo akabwera patsogolo pa guwa lansembe m’nyumba ino chifukwa cha zimene analumbira,

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena