Yoswa 10:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Choncho dzuwa linaimadi, ndiponso mwezi unaima mpaka mtunduwo utalanga adani ake.+ Kodi sizinalembedwe m’buku la Yasari?+ Dzuwa linaima kumwamba pakatikati, silinafulumire kulowa pafupifupi kwa tsiku lonse lathunthu.+ Oweruza 11:36 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 36 Koma iye anati: “Bambo, ngati mwatsegula pakamwa panu pamaso pa Yehova, ndichitireni mogwirizana ndi zimene zatuluka pakamwa panu,+ chifukwa Yehova wakugwirirani ntchito yobwezera adani anu, ana a Amoni.” Oweruza 16:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Ndiyeno Samisoni+ anafuulira Yehova,+ kuti: “Yehova Ambuye Wamkulu Koposa, chonde, ndikumbukireni+ ndi kundipatsa mphamvu+ kamodzi kokhaka, inu Mulungu woona. Ndiloleni ndiwabwezere Afilisiti chifukwa cha limodzi mwa maso anga awiriwa.”+
13 Choncho dzuwa linaimadi, ndiponso mwezi unaima mpaka mtunduwo utalanga adani ake.+ Kodi sizinalembedwe m’buku la Yasari?+ Dzuwa linaima kumwamba pakatikati, silinafulumire kulowa pafupifupi kwa tsiku lonse lathunthu.+
36 Koma iye anati: “Bambo, ngati mwatsegula pakamwa panu pamaso pa Yehova, ndichitireni mogwirizana ndi zimene zatuluka pakamwa panu,+ chifukwa Yehova wakugwirirani ntchito yobwezera adani anu, ana a Amoni.”
28 Ndiyeno Samisoni+ anafuulira Yehova,+ kuti: “Yehova Ambuye Wamkulu Koposa, chonde, ndikumbukireni+ ndi kundipatsa mphamvu+ kamodzi kokhaka, inu Mulungu woona. Ndiloleni ndiwabwezere Afilisiti chifukwa cha limodzi mwa maso anga awiriwa.”+