Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 16:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndipo m’mawa mudzaona ulemerero wa Yehova+ chifukwa wamva kung’ung’udza kwanu kotsutsana ndi Yehovayo. Ife ndife ndani kuti muziting’ung’udzira?”

  • Numeri 14:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Koma khamu lonselo linayamba kunena zoti liwaponye miyala.+ Kenako, ulemerero wa Yehova unaonekera kwa ana a Isiraeli onse pamwamba pa chihema chokumanako.+

  • Numeri 16:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Kora atasonkhanitsa khamu+ lonse lotsutsana nawo pakhomo la chihema chokumanako, ulemerero wa Yehova unaonekera kwa khamu lonselo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena