Numeri 21:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Pamenepo Yehova anatumiza njoka zapoizoni pakati pawo,+ ndipo zinayamba kuwaluma moti Aisiraeli ambiri anafa.+ Yeremiya 8:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 “Inetu ndikutumiza njoka pakati panu, njoka zapoizoni,+ zimene simungaziimbire nyimbo kuti muziseweretse,+ ndipo zidzakulumani ndithu,” watero Yehova. Amosi 9:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Akabisala pamwamba pa phiri la Karimeli, ndidzawafufuza mosamala ndi kuwatenga,+ ndipo akathawa pamaso panga ndi kubisala pansi pa nyanja,+ ndidzalamula njoka pansi pa nyanja pomwepo kuti iwalume.
6 Pamenepo Yehova anatumiza njoka zapoizoni pakati pawo,+ ndipo zinayamba kuwaluma moti Aisiraeli ambiri anafa.+
17 “Inetu ndikutumiza njoka pakati panu, njoka zapoizoni,+ zimene simungaziimbire nyimbo kuti muziseweretse,+ ndipo zidzakulumani ndithu,” watero Yehova.
3 Akabisala pamwamba pa phiri la Karimeli, ndidzawafufuza mosamala ndi kuwatenga,+ ndipo akathawa pamaso panga ndi kubisala pansi pa nyanja,+ ndidzalamula njoka pansi pa nyanja pomwepo kuti iwalume.