Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 68:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Vomerezani kuti Mulungu ndi wamphamvu zochuluka.+

      Iye akulamulira Isiraeli ndipo mphamvu zake zili m’mitambo.+

  • Salimo 93:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 93 Yehova wakhala mfumu!+

      Iye wavala ulemerero.+

      Yehova wavala mphamvu ngati chovala, ndipo wamangirira mphamvuzo m’chiuno mwake.+

      Dziko lapansi lakhazikika, moti silingagwedezeke.+

  • Salimo 104:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu munamanga zipinda za m’mwamba pamadzi pogwiritsa ntchito mitanda,+

      Munapanga mitambo kukhala galeta lanu,+

      Mumayenda pamapiko a mphepo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena