Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 20:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 “Usalakelake nyumba ya mnzako. Usalakelake mkazi wa mnzako,+ kapolo wake wamwamuna, kapolo wake wamkazi, ng’ombe yake, bulu wake, kapena chilichonse cha mnzako.”+

  • 1 Mafumu 21:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 Choncho Ahabu analowa m’nyumba mwake ali wachisoni ndi wokhumudwa chifukwa cha mawu amene Naboti Myezereeli anamuuza, onena kuti: “Sindikupatsani cholowa cha makolo anga.” Ndiyeno anakagona pabedi lake n’kutembenukira kukhoma,+ ndipo sanadye chakudya.

  • Luka 12:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Kenako anauza anthuwo kuti: “Khalani maso ndipo chenjerani ndi kusirira kwa nsanje kwamtundu uliwonse,+ chifukwa ngakhale munthu atakhala ndi zochuluka chotani, moyo wake suchokera m’zinthu zimene ali nazo.”+

  • Aroma 7:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Ndiye tinene kuti chiyani? Kodi Chilamulo ndi uchimo?+ Ayi m’pang’ono pomwe! Kunena zoona, sindikanadziwa uchimo+ zikanakhala kuti panalibe Chilamulo. Ndiponso, mwachitsanzo, sindikanadziwa kusirira kwa nsanje+ zikanakhala kuti Chilamulo sichinanene kuti: “Usasirire mwansanje.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena