Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 78:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pakuti iwo sanakhulupirire Mulungu.+

      Sanakhulupirire kuti iye adzawapulumutsa.+

  • Salimo 106:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Iwo anayamba kunyansidwa ndi dziko losiririka,+

      Ndipo analibe chikhulupiriro m’mawu ake.+

  • Aheberi 3:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Kodi paja ndi ndani amene anamva koma n’kupsetsa mtima Mulungu?+ Kodi si anthu onse amene anatuluka m’dziko la Iguputo motsogoleredwa ndi Mose?+

  • Aheberi 3:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Choncho, tikuona kuti sakanatha kulowa mu mpumulowo chifukwa anali opanda chikhulupiriro.+

  • Yuda 5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ngakhale kuti mukudziwa kale zinthu zonse, ndikufuna kukukumbutsani kuti,+ ngakhale kuti Yehova anapulumutsa anthu ake powatulutsa m’dziko la Iguputo,+ pambuyo pake anawononga amene analibe chikhulupiriro.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena