Ekisodo 23:23 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 23 Pakuti mngelo wanga adzakutsogolera ndi kukulowetsa m’dziko la Aamori, Ahiti, Aperezi, Akanani, Ahivi ndi Ayebusi, ndipo ndidzawafafaniza ndithu.+ Deuteronomo 9:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Ndipo inu mukudziwa bwino lero kuti Yehova Mulungu wanu akuwoloka patsogolo panu+ kuti akutsogolereni. Iye ndi moto wowononga.+ Adzawawononga+ ndipo iye ndi amene adzawagonjetsa inu mukuona. Pamenepo mudzawalande dziko lawo ndi kuwawononga mofulumira monga mmene Yehova wakuuzirani.+ Deuteronomo 19:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 “Yehova Mulungu wako akadzawononga mitundu+ ya m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, iwe n’kuwalandadi dzikolo ndi kukhala m’mizinda yawo ndi m’nyumba zawo,+ Salimo 44:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Munapitikitsa anthu a mitundu ina ndi dzanja lanu,+Ndipo m’malo mwawo munakhazikitsa anthu anu.+Munagonjetsa mitundu ya anthu ndi kuipitikitsa.+ Salimo 78:55 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 55 Chifukwa cha iwo anachotsa mitundu ina pang’onopang’ono m’dzikoli,+Ndipo anayesa dzikoli ndi kuligawa kwa iwo kukhala cholowa chawo,+Moti anachititsa mafuko a Isiraeli kukhala m’nyumba zawozawo.+
23 Pakuti mngelo wanga adzakutsogolera ndi kukulowetsa m’dziko la Aamori, Ahiti, Aperezi, Akanani, Ahivi ndi Ayebusi, ndipo ndidzawafafaniza ndithu.+
3 Ndipo inu mukudziwa bwino lero kuti Yehova Mulungu wanu akuwoloka patsogolo panu+ kuti akutsogolereni. Iye ndi moto wowononga.+ Adzawawononga+ ndipo iye ndi amene adzawagonjetsa inu mukuona. Pamenepo mudzawalande dziko lawo ndi kuwawononga mofulumira monga mmene Yehova wakuuzirani.+
19 “Yehova Mulungu wako akadzawononga mitundu+ ya m’dziko limene Yehova Mulungu wako akukupatsa, iwe n’kuwalandadi dzikolo ndi kukhala m’mizinda yawo ndi m’nyumba zawo,+
2 Munapitikitsa anthu a mitundu ina ndi dzanja lanu,+Ndipo m’malo mwawo munakhazikitsa anthu anu.+Munagonjetsa mitundu ya anthu ndi kuipitikitsa.+
55 Chifukwa cha iwo anachotsa mitundu ina pang’onopang’ono m’dzikoli,+Ndipo anayesa dzikoli ndi kuligawa kwa iwo kukhala cholowa chawo,+Moti anachititsa mafuko a Isiraeli kukhala m’nyumba zawozawo.+