Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 36:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Chotero Esau anakakhazikika kudera lamapiri ku Seiri.+ Esau analinso kutchedwa Edomu.+

  • Numeri 20:14
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 14 Tsiku lina Mose anatumiza amithenga kuchokera ku Kadesi kumene iwo anali, kupita kwa mfumu ya Edomu,+ kukanena kuti: “Abale anu Aisiraeli+ akuti, ‘Inu mukudziwa bwino za mavuto onse amene ationekera ife.+

  • Deuteronomo 23:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Usaipidwe ndi Mwedomu, chifukwa ndi m’bale wako.+

      “Usaipidwe ndi Mwiguputo, chifukwa unali mlendo m’dziko lawo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena