Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 23:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Sara anamwalirira ku Kiriyati-ariba,+ kapena kuti ku Heburoni,+ m’dziko la Kanani.+ Pamenepo Abulahamu analowa muhema kukamulira Sara.

  • Genesis 35:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Potsirizira pake Yakobo anafika kwa bambo ake Isaki ku Mamure,+ m’dera la Kiriyati-ariba,+ komwe ndi ku Heburoni. Uku n’kumenenso Abulahamu ndi Isaki anakhalako monga alendo.+

  • Yoswa 15:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kalebe+ mwana wa Yefune anam’patsa gawo lake pakati pa ana a Yuda pomvera lamulo la Yehova kwa Yoswa. Anam’patsa Kiriyati-ariba, kutanthauza Heburoni.+ (Ariba anali tate wa Anaki.)

  • Oweruza 1:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Motero fuko la Yuda linapita kukamenyana ndi Akanani amene anali kukhala ku Heburoni,+ (poyamba dzina la mzinda wa Heburoni linali Kiriyati-ariba).+ Iwo anapha Sesai, Ahimani ndi Talimai.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena