Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 19:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 “Uza khamu lonse la ana a Isiraeli kuti, ‘Mukhale oyera,+ chifukwa ine Yehova Mulungu wanu ndine woyera.+

  • 1 Samueli 6:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Kenako amuna a ku Beti-semesi ananena kuti: “Ndani angaime pamaso pa Yehova Mulungu woyera,+ ndipo kodi sangatileke n’kupita kwa ena?”+

  • Salimo 99:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Kwezani Yehova Mulungu wathu+ ndipo muweramireni pachopondapo mapazi ake.+

      Iye ndi woyera.+

  • Yesaya 6:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Aliyense anali kuuza mnzake kuti: “Woyera, woyera, woyera ndiye Yehova wa makamu.+ Zonse zimene zili padziko lapansi zimasonyeza ulemerero wake.”

  • 1 Petulo 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Koma khalani motsanzira Woyera amene anakuitanani. Inunso khalani oyera m’makhalidwe anu onse,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena