Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 17:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsopano ana a Isiraeli anayamba kuuza Mose kuti: “Tsopano ife tifa ndithu! Ndithudi titha ife! Tonse titha basi.+

  • 2 Samueli 6:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsiku limenelo, Davide anachita mantha kwambiri chifukwa cha Yehova,+ ndipo anati: “Kodi likasa la Yehova lidzabwera bwanji kumene ine ndikukhala?”+

  • 1 Mbiri 13:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Tsiku limenelo, Davide anachita mantha kwambiri chifukwa cha Mulungu woona,+ ndipo anati: “Kodi ndibweretsa bwanji likasa la Mulungu woona kumene ine ndikukhala?”+

  • Salimo 76:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Inu ndinu wochititsa mantha,+

      Ndani angaime pamaso panu inu mutakwiya kwambiri?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena