Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 32:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pamapeto pake ndinaulula tchimo langa kwa inu, ndipo sindinabise cholakwa changa.+

      Ndinati: “Ndidzaulula kwa Yehova machimo anga.”+

      Ndipo inu munandikhululukira zolakwa zanga ndi machimo anga.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 51:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ine ndakuchimwirani kwambiri,+

      Ndipo ndachita chinthu choipa pamaso panu,+

      Choncho mukamalankhula mumalankhula zachilungamo,+

      Ndipo mukamaweruza, mumaweruza molungama.+

  • 1 Timoteyo 5:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Machimo a anthu ena amaonekera poyera,+ ndipo zimenezi zimachititsa kuti aweruzidwe. Koma anthu ena, machimo awo amadzaonekera pambuyo pake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena