Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Levitiko 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 “‘Ndipo akadziwa kuti wapalamula mlandu pa chilichonse mwa zimenezi, pamenepo aziulula+ kuti wachimwa motani.

  • 2 Samueli 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pamenepo Davide anauza+ Natani kuti: “Ndachimwira Yehova.”+ Ndiyeno Natani anauza Davide kuti: “Yehova wakukhululukira tchimo lako+ ndipo suufa.+

  • 2 Mbiri 30:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Kuwonjezera apo, Hezekiya analankhula mokoma mtima+ kwa Alevi onse amene anali kutumikira Yehova mwanzeru.+ Anthuwo anachita phwando loikidwiratu kwa masiku 7.+ Anali kupereka nsembe zachiyanjano+ ndi kulapa+ kwa Yehova Mulungu wa makolo awo.

  • Salimo 38:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Pakuti ndinali kulankhula za cholakwa changa.+

      Ndipo ndinali kudera nkhawa za tchimo langa.+

  • Salimo 41:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Koma ine ndinati: “Inu Yehova, ndikomereni mtima.+

      Ndichiritseni, pakuti ndakuchimwirani.”+

  • Mateyu 3:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Iye anali kuwabatiza mumtsinje wa Yorodano,+ ndipo anthuwo anali kuulula machimo awo poyera.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena