Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 23:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Kenako Sauli anafika ndi asilikali ake kudzafunafuna Davide.+ Davide atauzidwa zimenezi, nthawi yomweyo analowa mkatikati mwa chipululu n’kukabisala kuthanthwe,+ ndipo anapitiriza kukhala m’chipululu cha Maoni. Sauli atamva zimenezo anayamba kuthamangitsa+ Davide m’chipululu chimenecho cha Maoni.

  • 1 Samueli 25:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 2 Tsopano mwamuna wina anali kukhala ku Maoni,+ koma ntchito yake anali kugwirira ku Karimeli.*+ Mwamuna ameneyu anali wotchuka kwambiri, ndipo anali ndi nkhosa 3,000 ndi mbuzi 1,000. Tsiku lina, iye anali kugwira ntchito yometa ubweya+ wa nkhosa zake ku Karimeli.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena