Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 19:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano mwamunayo+ anaimirira kuti azipita, iyeyo pamodzi ndi mdzakazi wake+ ndiponso mtumiki wake,+ koma apongozi ake, bambo a mtsikanayo, anamuuza kuti: “Anotu ndi madzulo tsopano, ndipo posachedwa kuchita mdima. Chonde, lero mugone kuno.+ Onani, kunja kwatsala pang’ono kuda. Lero mugone kuno ndipo musangalatse mtima wanu.+ Mawa mudzuke m’mawa kwambiri ndi kuyamba ulendo wanu wopita kuhema wanu.”

  • Oweruza 19:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pamene anali kusangalatsa mitima yawo,+ mwadzidzidzi amuna a mumzindawo, anthu opanda pake,+ anazungulira nyumbayo,+ ndipo anali kukankhanakankhana pachitseko. Iwo anali kuuza mwamuna wokalamba uja, mwini nyumbayo, kuti: “Tulutsa mwamuna amene wabwera m’nyumba yako kuti tigone naye.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena