Yoswa 18:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Mizinda ya fuko la ana a Benjamini potsata mabanja awo inali Yeriko,+ Beti-hogila, Emeki-kezizi, Yoswa 18:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Zela,+ Ha-elefi, Yebusi, kutanthauza Yerusalemu,+ Gibea,+ ndi Kiriyati. Mizinda 14 ndi midzi yake. Ichi chinali cholowa cha ana a Benjamini potsata mabanja awo.+
28 Zela,+ Ha-elefi, Yebusi, kutanthauza Yerusalemu,+ Gibea,+ ndi Kiriyati. Mizinda 14 ndi midzi yake. Ichi chinali cholowa cha ana a Benjamini potsata mabanja awo.+