Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 3:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo ana a Isiraeli anayamba kufuulira Yehova kuti awathandize.+ Pamenepo Yehova anapereka mpulumutsi+ wa ana a Isiraeli kuti awapulumutse. Ameneyu anali Otiniyeli,+ mwana wamwamuna wa Kenazi,+ mng’ono wake wa Kalebe.+

  • Salimo 50:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pa tsiku la nsautso undiitane.+

      Ine ndidzakulanditsa, ndipo iwe udzandilemekeza.”+

  • Salimo 78:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Nthawi zonse akayamba kuwapha, iwo anali kumufunafuna.+

      Anali kutembenuka ndi kuyamba kufunafuna Mulungu.+

  • Salimo 107:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iwo anayamba kuitana Yehova kuti awathandize m’masautso awo,+

      Ndipo iye anawapulumutsa ku mavuto awo monga mwa nthawi zonse.+

  • Yeremiya 29:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 ‘Mudzaitanira pa ine komanso mudzabwera ndi kupemphera kwa ine ndipo ine ndidzakumvetserani.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena