Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Yaeli,+ mkazi wa Hiberi Mkeni,+ akhale wodalitsika pakati pa akazi onse,

      Akhale wodalitsika pakati pa akazi onse okhala m’mahema.+

  • Oweruza 5:26
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 26 Kenako anatambasula dzanja lake ndi kugwira chikhomo cha hema.

      Anatambasulanso dzanja lake lamanja ndi kutenga nyundo yamtengo, ya anthu ogwira ntchito mwamphamvu.+

      Atatero anakhoma Sisera m’mutu ndipo chikhomocho chinatulukira mbali ina ya mutu wakewo.+

      Anaphwanya ndi kudula fupa la pafupi ndi khutu la Sisera.

  • Oweruza 9:54
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 54 Msangamsanga Abimeleki anaitana mtumiki wake womunyamulira zida ndi kumuuza kuti: “Tenga lupanga lako undiphe,+ kuopera kuti anthu anganene za ine kuti, ‘Anaphedwa ndi mkazi.’” Nthawi yomweyo, mtumiki wakeyo anamubaya* ndi lupanga, ndipo anafa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena