Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 4:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Pamenepo Debora anati: “Sindilephera, tipitira limodzi. Ngakhale zili choncho, ulemerero sukhala wako kumene ukupitako, chifukwa Yehova adzapereka Sisera m’manja mwa munthu wamkazi.”+ Atatero, Debora ananyamuka n’kutsagana ndi Baraki ku Kedesi.+

  • Oweruza 5:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Sisera anakomoka, kugwa ndi kugona pakati pa mapazi ake,

      Iye anakomoka n’kugwa.

      Pamene anakomokerapo, anagwera pomwepo, atagonja.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena