Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 68:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Monga mmene mphepo imauluzira utsi, inunso muwauluze chimodzimodzi.+

      Ngati mmene phula limasungunukira chifukwa cha moto,+

      Anthu oipa awonongeke ndi kuchotsedwa pamaso pa Mulungu.+

  • Salimo 83:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Muwachitire zimene munachitira Midiyani+ ndi Sisera.+

      Muwachitirenso zimene munachitira Yabini+ kuchigwa cha Kisoni.+

  • Salimo 92:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti taonani adani anu, inu Yehova!+

      Adani anu onse adzatha!+

      Anthu onse ochita zopweteka anzawo adzamwazikana.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena