Numeri 31:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Amunawo anakathira nkhondo Amidiyani, monga mmene Yehova analamulira Mose, ndipo anapha mwamuna aliyense.+ Oweruza 8:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Pamenepa n’kuti Zeba ndi Zalimuna+ ali ku Karikori pamodzi ndi asilikali awo okwana pafupifupi 15,000. Asilikaliwa ndi amene anatsala pa gulu lonse la asilikali a Kum’mawa,+ ndipo amene anali ataphedwa anali asilikali 120,000.+ Yesaya 9:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Pakuti goli la katundu wawo,+ ndodo yomwe inali pamapewa awo, ndiponso ndodo ya amene anali kuwakusira ku ntchito,+ mwazithyolathyola ngati pa tsiku limene Amidiyani anagonjetsedwa.+ Yesaya 10:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Yehova wa makamu adzam’kwapula ndi chikwapu+ ngati mmene anagonjetsera Midiyani pathanthwe la Orebi.+ Ndodo yake idzakhala panyanja+ ndipo adzaikweza m’mwamba ngati mmene anachitira ndi Iguputo.+
7 Amunawo anakathira nkhondo Amidiyani, monga mmene Yehova analamulira Mose, ndipo anapha mwamuna aliyense.+
10 Pamenepa n’kuti Zeba ndi Zalimuna+ ali ku Karikori pamodzi ndi asilikali awo okwana pafupifupi 15,000. Asilikaliwa ndi amene anatsala pa gulu lonse la asilikali a Kum’mawa,+ ndipo amene anali ataphedwa anali asilikali 120,000.+
4 Pakuti goli la katundu wawo,+ ndodo yomwe inali pamapewa awo, ndiponso ndodo ya amene anali kuwakusira ku ntchito,+ mwazithyolathyola ngati pa tsiku limene Amidiyani anagonjetsedwa.+
26 Yehova wa makamu adzam’kwapula ndi chikwapu+ ngati mmene anagonjetsera Midiyani pathanthwe la Orebi.+ Ndodo yake idzakhala panyanja+ ndipo adzaikweza m’mwamba ngati mmene anachitira ndi Iguputo.+