Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 40:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Iwo anamuyankha kuti: “Talota maloto, koma palibe wotimasulira malotowo.” Pamenepo Yosefe anawauza kuti: “Kodi Mulungu sindiye amamasulira?+ Tandifotokozerani malotowo.”

  • Oweruza 7:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Kumeneko ukamvetsere zolankhula zawo.+ Pambuyo pake udzalimba mtima+ ndipo udzapitadi kumsasawo ndi kuuthira nkhondo.” Pamenepo, Gidiyoni ndi Pura mtumiki wake, anapita kumunsi pafupi kwambiri ndi asilikali amene anafola mwa dongosolo lomenyera nkhondo amene anali mumsasawo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena