Yoswa 6:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Ndipo Rahabi hule uja, limodzi ndi anthu a m’nyumba ya bambo ake, ndi onse amene anali naye, Yoswa sanawaphe.+ Kufikira lero, mayiyo akukhalabe pakati pa Aisiraeli,+ chifukwa anabisa anyamata amene Yoswa anawatuma kukazonda Yeriko.+ 1 Samueli 15:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Zili choncho, Sauli anauza Akeni+ kuti: “Nyamukani,+ muchoke pakati pa Aamaleki kuti ndisakuwonongeni pamodzi nawo. Inuyo munasonyeza kukoma mtima kosatha kwa ana onse a Isiraeli+ atatuluka mu Iguputo.”+ Choncho Akeni anachokadi pakati pa Aamaleki.
25 Ndipo Rahabi hule uja, limodzi ndi anthu a m’nyumba ya bambo ake, ndi onse amene anali naye, Yoswa sanawaphe.+ Kufikira lero, mayiyo akukhalabe pakati pa Aisiraeli,+ chifukwa anabisa anyamata amene Yoswa anawatuma kukazonda Yeriko.+
6 Zili choncho, Sauli anauza Akeni+ kuti: “Nyamukani,+ muchoke pakati pa Aamaleki kuti ndisakuwonongeni pamodzi nawo. Inuyo munasonyeza kukoma mtima kosatha kwa ana onse a Isiraeli+ atatuluka mu Iguputo.”+ Choncho Akeni anachokadi pakati pa Aamaleki.