Genesis 18:25 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 25 Simungachite zimenezo, kupha munthu wolungama limodzi ndi woipa. Sizingatheke kuti wolungama aone zofanana ndi woipa.+ Simungachite zimenezo ayi.+ Kodi Woweruza wa dziko lonse lapansi sadzachita cholungama?”+ Genesis 19:12 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 12 Ndiyeno alendowo anafunsa Loti kuti: “Kodi uli ndi achibale alionse kuno? Uwatulutse mumzinda uno,+ kaya ndi akamwini ako, ana ako aamuna, ana ako aakazi, kapena alionse amene ndi abale ako. Numeri 16:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Atafika anauza khamulo kuti: “Chonde, chokani kumahema a anthu oipawa, ndipo musakhudze chinthu chawo chilichonse,+ kuti musaphedwe nawo limodzi chifukwa cha kuchimwa kwawo.” 1 Mafumu 20:31 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 31 Ndiyeno atumiki ake anamuuza kuti: “Tamva kuti mafumu a nyumba ya Isiraeli ndiwo mafumu amene amasonyeza kukoma mtima kosatha.+ Tiyeni tivale ziguduli*+ m’chiuno mwathu+ ndi kumanga zingwe kumutu kwathu, kuti tipite kwa mfumu ya Isiraeli. Mwina sikakuphani.”+ Miyambo 20:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Kukoma mtima kosatha ndiponso choonadi zimateteza mfumu,+ ndipo chifukwa cha kukoma mtima kosatha kumeneko mfumu imakhazikitsa mpando wake wachifumu.+
25 Simungachite zimenezo, kupha munthu wolungama limodzi ndi woipa. Sizingatheke kuti wolungama aone zofanana ndi woipa.+ Simungachite zimenezo ayi.+ Kodi Woweruza wa dziko lonse lapansi sadzachita cholungama?”+
12 Ndiyeno alendowo anafunsa Loti kuti: “Kodi uli ndi achibale alionse kuno? Uwatulutse mumzinda uno,+ kaya ndi akamwini ako, ana ako aamuna, ana ako aakazi, kapena alionse amene ndi abale ako.
26 Atafika anauza khamulo kuti: “Chonde, chokani kumahema a anthu oipawa, ndipo musakhudze chinthu chawo chilichonse,+ kuti musaphedwe nawo limodzi chifukwa cha kuchimwa kwawo.”
31 Ndiyeno atumiki ake anamuuza kuti: “Tamva kuti mafumu a nyumba ya Isiraeli ndiwo mafumu amene amasonyeza kukoma mtima kosatha.+ Tiyeni tivale ziguduli*+ m’chiuno mwathu+ ndi kumanga zingwe kumutu kwathu, kuti tipite kwa mfumu ya Isiraeli. Mwina sikakuphani.”+
28 Kukoma mtima kosatha ndiponso choonadi zimateteza mfumu,+ ndipo chifukwa cha kukoma mtima kosatha kumeneko mfumu imakhazikitsa mpando wake wachifumu.+