Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 45:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Aliyense wa iwo anam’patsa chovala choti asinthire,+ koma Benjamini anam’patsa zovala zosinthira zisanu, ndi ndalama zasiliva 300.+

  • Oweruza 14:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pamenepo mzimu wa Yehova unayamba kugwira ntchito pa iye.+ Choncho anapita ku Asikeloni+ kumene anakapha amuna 30, ndipo anatenga zovala zawo n’kuzipereka kwa amene anamasulira mwambi aja.+ Koma mkwiyo wake unapitiriza kuyaka, ndipo anapita kunyumba ya bambo ake.

  • 2 Mafumu 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ndiyeno mfumu ya Siriya inauza Namani kuti: “Nyamuka, ndikupatsa kalata upite kwa mfumu ya Isiraeli.” Choncho iye ananyamuka atatenga+ matalente* 10 a siliva, masekeli 6,000 a golide,+ ndi zovala 10.+

  • 2 Mafumu 5:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Gehazi anayankha kuti: “Inde n’kwabwino. Mbuyanga+ wandituma+ kuti, ‘Posachedwapa kwabwera anyamata awiri, ana a aneneri,+ kuchokera kudera lamapiri la Efuraimu. Muwapatseko talente imodzi ya siliva ndi zovala ziwiri.’”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena