Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 36:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Nawa tsopano mafumu aakulu amene analamulira dziko la Edomu,+ ana a Isiraeli asanayambe kulamulidwa ndi mfumu ina iliyonse:+

  • Deuteronomo 33:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu anakhala mfumu mu Yesuruni,*+

      Pamene atsogoleri a anthu anasonkhana pamodzi,+

      Chiwerengero chonse cha mafuko a Isiraeli.+

  • Oweruza 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Masiku amenewo mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Ndipo m’masiku amenewo fuko la Dani+ linali kufuna cholowa chake kuti likakhale kumeneko, chifukwa mpaka pa nthawi imeneyi linali lisanalandirebe cholowa pakati pa mafuko onse a Isiraeli.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena