Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 36:31
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 31 Nawa tsopano mafumu aakulu amene analamulira dziko la Edomu,+ ana a Isiraeli asanayambe kulamulidwa ndi mfumu ina iliyonse:+

  • Deuteronomo 33:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mulungu anakhala mfumu mu Yesuruni,*+

      Pamene atsogoleri a anthu anasonkhana pamodzi,+

      Chiwerengero chonse cha mafuko a Isiraeli.+

  • Oweruza 8:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Koma Gidiyoni anawayankha kuti: “Ineyo sindikhala wokulamulirani, ngakhalenso mwana wanga sakhala wokulamulirani.+ Yehova ndiye azikulamulirani.”+

  • Oweruza 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Masiku amenewo mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Aliyense anali kuchita zimene anali kuona kuti n’zoyenera.+

  • Oweruza 19:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Tsopano masiku amenewo, mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Ndiyeno Mlevi wina anakhala kwa kanthawi m’dera lamapiri lakutali kwambiri la Efuraimu.+ Patapita nthawi, anatenga mkazi wa ku Betelehemu,+ ku Yuda, kukhala mdzakazi wake.+

  • Oweruza 21:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Masiku amenewo mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Aliyense anali kuchita zimene anali kuona kuti n’zoyenera.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena