Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 12:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 “Musakachite zimene tikuchita kuno lero, aliyense kumangochita zimene akufuna,+

  • Deuteronomo 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 “Mudziikire oweruza+ ndi atsogoleri+ m’mizinda yanu yonse imene Yehova Mulungu wanu akukupatsani, malinga ndi mafuko anu. Oweruza ndi atsogoleriwo aziweruza anthu ndi chiweruzo cholungama.

  • Oweruza 17:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Masiku amenewo mu Isiraeli munalibe mfumu.+ Aliyense anali kuchita zimene anali kuona kuti n’zoyenera.+

  • 1 Samueli 9:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Samueli ataona Sauli, Yehova anamuuza kuti: “Ameneyu ndiye munthu ndimakuuza uja kuti, ‘Ameneyo ndiye adzalamulire anthu anga.’”+

  • Miyambo 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Khulupirira Yehova ndi mtima wako wonse,+ ndipo usadalire luso lako lomvetsa zinthu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena